Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 12:31 - Buku Lopatulika

31 Komatu tafunafunani Ufumu wake, ndipo izi adzakuonjezerani.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

31 Komatu tafunafunani Ufumu wake, ndipo izi adzakuonjezerani.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

31 Koma inu, yambani mwafunafuna ufumu wa Mulungu, ndipo zina zonsezi adzakupatsaninso.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

31 Koma funafunani ufumu wake, ndipo mudzapatsidwa zonsezi.

Onani mutuwo Koperani




Luka 12:31
14 Mawu Ofanana  

Opani Yehova, inu oyera mtima ake; chifukwa iwo akumuopa Iye sasowa.


Sadzachita manyazi m'nyengo yoipa, ndipo m'masiku a njala adzakhuta.


Ndinali mwana ndipo ndakalamba; ndipo sindinapenye wolungama atasiyidwa, kapena mbumba zake zilinkupempha chakudya.


Khulupirira Yehova, ndipo chita chokoma; khala m'dziko, ndipo tsata choonadi.


Pakuti Yehova Mulungu ndiye dzuwa ndi chikopa; Yehova adzapatsa chifundo ndi ulemerero; sadzakaniza chokoma iwo akuyenda angwiro.


iye adzakhala pamsanje; malo ake ochinjikiza adzakhala malinga amiyala; chakudya chake chidzapatsidwa kwa iye; madzi ake adzakhala chikhalire.


Koma muyambe mwafuna Ufumu wake ndi chilungamo chake, ndipo zonse zimenezo zidzaonjezedwa kwa inu.


koma chisoweka chinthu chimodzi, pakuti Maria anasankha dera lokoma limene silidzachotsedwa kwa iye.


Pakuti izi zonse mitundu ya anthu a padziko lapansi amazifunafuna; koma Atate wanu adziwa kuti musowa zimenezi.


Gwirani ntchito si chifukwa cha chakudya chimene chitayika koma cha chakudya chimene chitsalira kumoyo wosatha, chimene Mwana wa Munthu adzakupatsani inu; pakuti ameneyo Atate, ndiye Mulungu, adamlembera chizindikiro.


Ndipo tidzatani ndi zinthu izi? Ngati Mulungu ali ndi ife, adzatikaniza ndani?


pakuti chizolowezi cha thupi chipindula pang'ono, koma chipembedzo chipindula zonse, popeza chikhala nalo lonjezano la kumoyo uno, ndi la moyo ulinkudza.


Mtima wanu ukhale wosakonda chuma; zimene muli nazo zikukwanireni; pakuti Iye anati, Sindidzakusiya konse, kungakhale kukutaya, sindidzakutaya ndithu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa