Luka 12:31 - Buku Lopatulika31 Komatu tafunafunani Ufumu wake, ndipo izi adzakuonjezerani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Komatu tafunafunani Ufumu wake, ndipo izi adzakuonjezerani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Koma inu, yambani mwafunafuna ufumu wa Mulungu, ndipo zina zonsezi adzakupatsaninso.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Koma funafunani ufumu wake, ndipo mudzapatsidwa zonsezi. Onani mutuwo |