Luka 12:25 - Buku Lopatulika25 Ndipo ndani wa inu, ndi kuda nkhawa angathe kuonjeza mkono pa msinkhu wake? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Ndipo ndani wa inu, ndi kuda nkhawa angathe kuonjeza mkono pa msinkhu wake? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Ndani mwa inu ndi maganizo ankhaŵa angathe kuwonjezera ngakhale tsiku limodzi pa moyo wake? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Ndi ndani wa inu akhoza kuwonjeza ora pa moyo wake chifukwa cha kudandaula? Onani mutuwo |