Luka 12:26 - Buku Lopatulika26 Kotero ngati simungathe ngakhale chaching'onong'ono, muderanji nkhawa chifukwa cha zina zija? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Kotero ngati simungathe ngakhale chaching'onong'ono, muderanji nkhawa chifukwa cha zina zija? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Tsono ngati simungathe kuchita ngakhale kanthu kakang'ono kotere, bwanji mukudera nkhaŵa zinazo? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Popeza simungathe kuchita kanthu kakangʼono aka, nʼchifukwa chiyani mumadandaula ndi zinazi? Onani mutuwo |