Luka 12:14 - Buku Lopatulika14 Koma anati kwa iye, Munthu iwe, ndani anandiika Ine ndikhale woweruza, kapena wakugawira inu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Koma anati kwa iye, Munthu iwe, ndani anandiika Ine ndikhale woweruza, kapena wakugawira inu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Koma Yesu adati, “Munthu iwe, ndani adandipatsa ntchito yokuweruzani kapena kumakugaŵirani chuma chanu chamasiye?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Yesu anayankha kuti, “Munthu iwe, ndani anandiyika Ine kukhala woweruza kapena wogawa chuma pakati panu?” Onani mutuwo |