Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 11:54 - Buku Lopatulika

54 namlindira akakole kanthu kotuluka m'kamwa mwake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

54 namlindira akakole kanthu kotuluka m'kamwa mwake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

54 Cholinga chao chinali chofuna kumtapa m'kamwa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

54 pofuna kumukola muchina chilichonse chimene Iye angayankhule.

Onani mutuwo Koperani




Luka 11:54
12 Mawu Ofanana  

Ndipo kunali atawerenga kalatayo mfumu ya Israele, anang'amba zovala zake, nati, Ngati ndine Mulungu, kupha ndi kubwezera moyo, kuti ameneyo atumiza kwa ine kumchiritsa munthu khate lake? Pakuti dziwani, nimupenye, kuti alikufuna chifukwa pa ine.


Pomwepo Afarisi anamuka, nakhala upo wakumkola Iye m'kulankhula kwake.


Koma Yesu anadziwa kuipa kwao, nati, Mundiyeseranji Ine, onyenga inu?


Ndipo mmodzi wa iwo, mphunzitsi wa malamulo, anamfunsa ndi kumuyesa Iye, nati,


Ndipo anatuma kwa Iye ena a Afarisi ndi a Aherode, kuti akamkole Iye m'kulankhula kwake.


Ndipo anamuyang'anira Iye, ngati adzamchiritsa tsiku la Sabata; kuti ammange mlandu.


Ndipo pamene Iye anatuluka m'menemo, alembi ndi Afarisi anayamba kumuumiriza Iye kolimba, ndi kumfunsa zinthu zambiri;


Ndipo anamyang'anira, natumiza ozonda, amene anadzionetsera ngati olungama mtima, kuti akamkole pa mau ake, kotero kuti akampereke Iye ku ukulu ndi ulamuliro wa kazembe.


Ndipo sanakhoze kugwira mauwo pamaso pa anthu; ndipo anazizwa ndi kuyankha kwake, nakhala chete.


Pamenepo musakopedwe nao; pakuti amlalira iye oposa makumi anai a iwo amene anadzitemberera okha kuti sadzadya kapena kumwa kufikira atamupha iye; ndipo akonzekeratu tsopano nayang'anira lonjezano lanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa