Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 11:5 - Buku Lopatulika

5 Ndipo anati kwa iwo, Ndani wa inu adzakhala ndi bwenzi lake, nadzapita kwa iye pakati pa usiku, nadzati kwa iye, Bwenzi, ndibwereke mikate itatu;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ndipo anati kwa iwo, Ndani wa inu adzakhala ndi bwenzi lake, nadzapita kwa iye pakati pa usiku, nadzati kwa iye, Bwenzi, ndibwereke mikate itatu;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Adaŵauzanso kuti, “Tangoganizani: wina mwa inu ali ndi bwenzi lake, nkupita kunyumba kwake pakati pa usiku, nakamuuza kuti, ‘Iwe mnzanga, kodi ungakhale ndi buledi mtatu?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Kenaka anawawuza kuti, “Tiyerekeze: Mmodzi mwa inu atakhala ndi bwenzi lake, ndipo iye nʼkupita ku nyumba yake pakati pa usiku, nakanena kuti, ‘Mnzanga, bwereke malofu atatu abuledi,

Onani mutuwo Koperani




Luka 11:5
3 Mawu Ofanana  

Ndipo mutikhululukire ife machimo athu; pakuti ifenso tikhululukira munthu yense wa mangawa athu. Ndipo musatitengere ife kokatiyesa.


popeza wandidzera bwenzi langa lochokera paulendo ndipo ndilibe chompatsa;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa