Luka 11:45 - Buku Lopatulika45 Ndipo mmodzi wa achilamulo anayankha, nanena kwa Iye, Mphunzitsi, ndi kunena izi, mutitonza ifenso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201445 Ndipo mmodzi wa achilamulo anayankha, nanena kwa Iye, Mphunzitsi, ndi kunena izi, mutitonza ifenso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa45 Apo katswiri wina wa Malamulo adati, “Aphunzitsi, mukamanena zimenezi, mukunyozatu ndi ife tomwe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero45 Mmodzi mwa akatswiri a Malamulo anamuyankha Iye nati, “Aphunzitsi, pamene mukunena zinthu izi, mukutinyoza ifenso?” Onani mutuwo |