Luka 11:22 - Buku Lopatulika22 koma pamene paliponse amdzera wakumposa mphamvu, nakamgonjetsa, amchotsera zida zake zonse zimene anazitama, nagawa zofunkha zake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 koma pamene paliponse amdzera wakumposa mphamvu, nakamlaka, amchotsera zida zake zonse zimene anazitama, nagawa zofunkha zake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Koma pakabwera wina wamphamvu zoposa, namgonjetsa, amalanda zida zimene ankazidalirazo, nkugaŵagaŵa katundu amene walandayo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Koma pakabwera wina wamphamvu zoposa namugonjetsa, amalanda zida zimene munthuyo amazidalirazo ndi kugawa katundu wake. Onani mutuwo |