Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 11:23 - Buku Lopatulika

23 Iye wosavomerezana ndi Ine atsutsana ndi Ine; ndipo iye wosasonkhanitsa pamodzi ndi Ine amwaza.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Iye wosavomerezana ndi Ine atsutsana ndi Ine; ndipo iye wosasonkhanitsa pamodzi ndi Ine amwaza.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 “Munthu wosavomerezana ndi Ine, ndiye kuti ngwotsutsana nane. Ndipo wosandithandiza kusonkhanitsa, ndiye kuti ameneyo ngwomwaza.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 “Munthu amene sali mbali yanga ndi wotsutsana nane. Ndipo wosandithandiza kusonkhanitsa, ameneyo ndi womwaza.

Onani mutuwo Koperani




Luka 11:23
5 Mawu Ofanana  

Iye wosakhala pamodzi ndi Ine akana Ine, ndi iye wosasonkhanitsa pamodzi ndi Ine amwazamwaza.


Pakuti iye wosatsutsana ndi ife athandizana nafe.


koma pamene paliponse amdzera wakumposa mphamvu, nakamgonjetsa, amchotsera zida zake zonse zimene anazitama, nagawa zofunkha zake.


Koma Yesu anati kwa iye, Musamletse, pakuti iye amene satsutsana nanu athandizana nanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa