Luka 11:20 - Buku Lopatulika20 Koma ngati Ine nditulutsa ziwanda ndi chala cha Mulungu, pamenepo Ufumu wa Mulungu wafikira inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Koma ngati Ine nditulutsa ziwanda ndi chala cha Mulungu, pamenepo Ufumu wa Mulungu wafikira inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Koma ngati Ine ndimatulutsa mizimu yoipa ndi mphamvu za Mulungu, ndiye kuti Mulungu wayamba kukhazikitsa ufumu wake pakati panu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Koma ngati ndimatulutsa ziwanda ndi mphamvu ya Mulungu, ndiye kuti ufumu wa Mulungu wafika pakati panu. Onani mutuwo |