Luka 11:16 - Buku Lopatulika16 Koma ena anamuyesa, nafuna kwa Iye chizindikiro chochokera Kumwamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Koma ena anamuyesa, nafuna kwa Iye chizindikiro chochokera Kumwamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Enanso pofuna kumuyesa, adampempha kuti aŵaonetse chizindikiro chozizwitsa chochokera kumwamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Ena anamuyesa pomufunsa chizindikiro chochokera kumwamba. Onani mutuwo |