Luka 11:15 - Buku Lopatulika15 Koma ena mwa iwo anati, Ndi Belezebulu mkulu wa ziwanda amatulutsa ziwanda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Koma ena mwa iwo anati, Ndi Belezebulu mkulu wa ziwanda amatulutsa ziwanda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Koma ena mwa iwo adati, “Mphamvu zimene iyeyu amatulutsira mizimu yoipazi nzochokera kwa Belezebulu, mkulu wa mizimu yoipayo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Koma ena mwa iwo anati, “Iye akutulutsa ziwanda ndi mphamvu ya Belezebabu mfumu ya ziwanda.” Onani mutuwo |