Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 10:32 - Buku Lopatulika

32 Momwemonso Mlevi, pofika pamenepo, ndi kumuona, anapita mbali ina.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

32 Momwemonso Mlevi, pofika pamenepo, ndi kumuona, anapita mbali ina.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

32 Chimodzimodzinso Mlevi wina adafika pamalopo, ndipo pamene adaona munthuyo, nayenso adangolambalala.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

32 Chimodzimodzinso, Mlevi wina pamene anafika pa malopo ndi kumuona, analambalalanso.

Onani mutuwo Koperani




Luka 10:32
8 Mawu Ofanana  

Ndiwakhaliranso chotonza; pakundiona apukusa mutu.


Mnzako, ndi mnzake wa atate wako, usawasiye; usanke kunyumba ya mbale wako tsiku la tsoka lako; mnansi wapafupi aposa mbale wakutali.


Kodi si ndiko kupatsa chakudya chako kwa anjala, ndi kuti ubwere nao kunyumba kwako aumphawi otayika? Pakuona wamaliseche kuti umveke, ndi kuti usadzibisire wekha a chibale chako?


Ndipo kudangotero kuti wansembe wina anatsika njirayo, ndipo pakumuona iye anapita mbali ina.


Koma Msamariya wina ali pa ulendo wake anadza pali iye; ndipo pakumuona, anagwidwa chifundo,


Koma Paulo anafuula ndi mau aakulu, nati, Usadzipweteka wekha; tonse tili muno.


Ndipo anamgwira Sostene, mkulu wa sunagoge, nampanda kumpando wachiweruziro. Ndipo Galio sanasamalire zimenezi.


Pakuti anthu adzakhala odzikonda okha, okonda ndalama, odzitamandira, odzikuza, amwano, osamvera akuwabala, osayamika,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa