Luka 10:32 - Buku Lopatulika32 Momwemonso Mlevi, pofika pamenepo, ndi kumuona, anapita mbali ina. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Momwemonso Mlevi, pofika pamenepo, ndi kumuona, anapita mbali ina. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Chimodzimodzinso Mlevi wina adafika pamalopo, ndipo pamene adaona munthuyo, nayenso adangolambalala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Chimodzimodzinso, Mlevi wina pamene anafika pa malopo ndi kumuona, analambalalanso. Onani mutuwo |