Luka 10:31 - Buku Lopatulika31 Ndipo kudangotero kuti wansembe wina anatsika njirayo, ndipo pakumuona iye anapita mbali ina. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Ndipo kudangotero kuti wansembe wina anatsika njirayo, ndipo pakumuona iye anapita mbali ina. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 “Ndiye zidangochitika kuti wansembe wina ankapita pa njira yomweyo. Pamene adaona munthu uja, adangolambalala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Wansembe ankapita pa njira yomweyo, ndipo ataona munthuyo, analambalala. Onani mutuwo |