Luka 10:33 - Buku Lopatulika33 Koma Msamariya wina ali pa ulendo wake anadza pali iye; ndipo pakumuona, anagwidwa chifundo, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201433 Koma Msamariya wina ali pa ulendo wake anadza pali iye; ndipo pakumuona, anagwidwa chifundo, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa33 Koma Msamariya wina, ali pa ulendo wake, adafikanso pamalo pomwepo. Pamene adaona munthu uja, adamumvera chisoni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero33 Koma Msamariya wina, ali pa ulendo wake, anafika pamene panali munthuyo; ndipo atamuona, anamva naye chisoni. Onani mutuwo |