Luka 1:72 - Buku Lopatulika72 Kuchitira atate athu chifundo, ndi kukumbukira pangano lake lopatulika; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201472 Kuchitira atate athu chifundo, ndi kukumbukira pangano lake lopatulika; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa72 Choncho Iye waŵachitiradi chifundo makolo athu akale, ndipo wakumbukira chipangano chake choyera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero72 kuonetsa chifundo kwa makolo athu ndi kukumbukira pangano lake loyera, Onani mutuwo |