Luka 1:71 - Buku Lopatulika71 chipulumutso cha adani athu, ndi padzanja la anthu onse amene atida ife. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201471 chipulumutso cha adani athu, ndi pa dzanja la anthu onse amene atida ife. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa71 Adaalonjeza kuti adzatipulumutsa kwa adani athu, ndi kwa onse odana nafe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero71 chipulumutso kuchoka kwa adani athu ndi kuchoka mʼdzanja la onse otida, Onani mutuwo |