Luka 1:68 - Buku Lopatulika68 Wolemekezeka Ambuye, Mulungu wa Israele; chifukwa Iye anayang'ana, nachitira anthu ake chiombolo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201468 Wolemekezeka Ambuye, Mulungu wa Israele; chifukwa Iye anayang'ana, nachitira anthu ake chiombolo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa68 “Atamandike Ambuye, Mulungu wa Aisraele, chifukwa adadzayendera anthu ao, ndi kudzaŵaombola. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero68 “Alemekezeke Ambuye, Mulungu wa Israeli chifukwa wabwera ndi kuwombola anthu ake. Onani mutuwo |