Luka 1:69 - Buku Lopatulika69 Ndipo Iye anatikwezera ife nyanga ya chipulumutso, mwa fuko la Davide mwana wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201469 Ndipo Iye anatikwezera ife nyanga ya chipulumutso, mwa fuko la Davide mwana wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa69 Adautsa wina, wa fuko la mtumiki wake Davide, kuti akhale Mpulumutsi wathu wamphamvu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero69 Iye wakweza nyanga yachipulumutso kwa ife mu nyumba ya mtumiki wake Davide. Onani mutuwo |