Luka 1:67 - Buku Lopatulika67 Ndipo atate wake Zekariya anadzazidwa ndi Mzimu Woyera, nanenera za Mulungu, nati, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201467 Ndipo atate wake Zekariya anadzazidwa ndi Mzimu Woyera, nanenera za Mulungu, nati, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa67 Tsono Zakariya, bambo wa Yohaneyo, adadzazidwa ndi Mzimu Woyera, nayamba kulankhula mau ochokera kwa Mulungu. Adati, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero67 Abambo ake, Zakariya, anadzazidwa ndi Mzimu Woyera ndipo ananenera kuti, Onani mutuwo |