Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 1:62 - Buku Lopatulika

62 Ndipo anakodola atate wake, afuna amutche dzina liti?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

62 Ndipo anakodola atate wake, afuna amutche dzina liti?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

62 Tsono adalankhula ndi bambo wake ndi manja, namufunsa kuti, “Mukufuna kuti timutche dzina lanji?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

62 Pamenepo anapanga zizindikiro kwa abambo ake kuti adziwe dzina limene akanakonda kumutcha mwanayo.

Onani mutuwo Koperani




Luka 1:62
2 Mawu Ofanana  

Koma m'mene iye anatulukamo, sanathe kulankhula nao; ndipo anazindikira kuti iye adaona masomphenya mu Kachisimo. Ndipo iye analinkukodola iwo, nakhalabe wosalankhula.


Ndipo iwo anati kwa iye, Palibe wina wa abale ako amene atchedwa dzina ili.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa