Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 1:61 - Buku Lopatulika

61 Ndipo iwo anati kwa iye, Palibe wina wa abale ako amene atchedwa dzina ili.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

61 Ndipo iwo anati kwa iye, Palibe wina wa abale ako amene atchedwa dzina ili.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

61 Pamenepo anthuwo adamuuza kuti, “Koma pakati pa abale anu palibe amene ali ndi dzina limeneli.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

61 Iwo anati kwa iye, “Palibe mmodzi mwa abale ake amene ali ndi dzina limeneli.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 1:61
3 Mawu Ofanana  

Ndipo amake anayankha, kuti, Iai; koma adzatchedwa Yohane.


Ndipo anakodola atate wake, afuna amutche dzina liti?


Kunali munthu, wotumidwa ndi Mulungu, dzina lake ndiye Yohane.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa