Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 1:56 - Buku Lopatulika

56 Ndipo Maria anakhala ndi iye ngati miyezi itatu, nabweranso kunyumba kwake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

56 Ndipo Maria anakhala ndi iye ngati miyezi itatu, nabweranso kunyumba kwake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

56 Maria atakhala ndi Elizabeti ngati miyezi itatu, adabwerera kwao.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

56 Mariya anakhala ndi Elizabeti pafupifupi miyezi itatu ndipo kenaka anabwerera kwawo.

Onani mutuwo Koperani




Luka 1:56
2 Mawu Ofanana  

(Monga analankhula kwa makolo athu) kwa Abrahamu ndi kwa mbeu yake kunthawi yonse.


Ndipo inakwanira nthawi ya Elizabeti, ya kubala kwake, ndipo anabala mwana wamwamuna.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa