Luka 1:57 - Buku Lopatulika57 Ndipo inakwanira nthawi ya Elizabeti, ya kubala kwake, ndipo anabala mwana wamwamuna. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201457 Ndipo inakwanira nthawi ya Elizabeti, ya kubala kwake, ndipo anabala mwana wamwamuna. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa57 Nthaŵi yakuti Elizabeti achire idakwana, ndipo adabala mwana wamwamuna. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero57 Itakwana nthawi yoti Elizabeti abereke, anabereka mwana wamwamuna. Onani mutuwo |