Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 1:57 - Buku Lopatulika

57 Ndipo inakwanira nthawi ya Elizabeti, ya kubala kwake, ndipo anabala mwana wamwamuna.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

57 Ndipo inakwanira nthawi ya Elizabeti, ya kubala kwake, ndipo anabala mwana wamwamuna.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

57 Nthaŵi yakuti Elizabeti achire idakwana, ndipo adabala mwana wamwamuna.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

57 Itakwana nthawi yoti Elizabeti abereke, anabereka mwana wamwamuna.

Onani mutuwo Koperani




Luka 1:57
7 Mawu Ofanana  

Mulungu sindiye munthu, kuti aname; kapena mwana wa munthu, kuti aleke; kodi anena, osachita?


Koma mngelo anati kwa iye, Usaope Zekariya, chifukwa kuti lamveka pemphero lako, ndipo mkazi wako Elizabeti adzakubalira mwana wamwamuna, ndipo udzamutcha dzina lake Yohane.


Masiku a Herode, mfumu ya Yudeya, kunali munthu wansembe, dzina lake Zakariya, wa gulu la ansembe la Abiya; ndi mkazi wake wa ana aakazi a fuko la Aroni, dzina lake Elizabeti.


Ndipo Maria anakhala ndi iye ngati miyezi itatu, nabweranso kunyumba kwake.


Ndipo anansi ake ndi abale ake anamva kuti Ambuye anakulitsa chifundo chake pa iye; nakondwera naye pamodzi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa