Luka 1:55 - Buku Lopatulika55 (Monga analankhula kwa makolo athu) kwa Abrahamu ndi kwa mbeu yake kunthawi yonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201455 (Monga analankhula kwa makolo athu) kwa Abrahamu ndi kwa mbeu yake kunthawi yonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa55 Izi ndi zomwe adaalonjeza kuti adzaŵachitira makolo athu akale aja, Abrahamu ndi zidzukulu zake mpaka muyaya.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero55 Kwa Abrahamu ndi zidzukulu zake ku nthawi zonse monga ananena kwa makolo athu.” Onani mutuwo |