Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 1:54 - Buku Lopatulika

54 Anathangatira Israele mnyamata wake, kuti akakumbukire chifundo,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

54 Anathangatira Israele mnyamata wake, kuti akakumbukire chifundo,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

54 Wadzathandiza anthu ake Aisraele, pokumbukira chifundo chake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

54 Iye anathandiza mtumiki wake Israeli, pokumbukira chifundo chake.

Onani mutuwo Koperani




Luka 1:54
16 Mawu Ofanana  

Mulungu ali m'kati mwake, sudzasunthika, Mulungu adzauthandiza mbandakucha.


Anakumbukira chifundo chake ndi chikhulupiriko chake kunyumba ya Israele; malekezero onse a dziko lapansi anaona chipulumutso cha Mulungu wathu.


Kumbukira zinthu izi, Yakobo; ndi Israele, pakuti iwe ndiwe mtumiki wanga; ndakuumba, iwe ndiwe mtumiki wanga, Israele, sindidzakuiwala.


Kodi Efuremu ndiye mwana wanga wokondedwa? Kodi ndiye mwana wokondweretsa? Nthawi zonse zoti ndimnenera zomtsutsa, pakuti ndimkumbukiranso ndithu; chifukwa chake mumtima mwanga ndimlirira; ndidzamchitiradi chifundo, ati Yehova.


Yehova anaonekera kwa ine kale, ndi kuti, Inde, ndakukonda iwe ndi chikondi chosatha; chifukwa chake ndakukoka iwe ndi kukukomera mtima.


Mudzapatsa kwa Yakobo choonadi, ndi kwa Abrahamu chifundo chimene munalumbirira makolo athu kuyambira masiku a kale lomwe.


Anawakhutitsa anjala ndi zinthu zabwino, ndipo eni chuma anawachotsa opanda kanthu.


(Monga analankhula kwa makolo athu) kwa Abrahamu ndi kwa mbeu yake kunthawi yonse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa