Luka 1:52 - Buku Lopatulika52 Iye anatsitsa mafumu pa mipando yao yachifumu, ndipo anakweza aumphawi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201452 Iye anatsitsa mafumu pa mipando yao yachifumu, ndipo anakweza aumphawi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa52 Mafumu amphamvu waŵatsitsa pa mipando yao yachifumu, anthu wamba nkuŵakweza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero52 Iye anachotsa olamulira pa mipando yawo yaufumu, koma wakweza odzichepetsa. Onani mutuwo |