Luka 1:51 - Buku Lopatulika51 Iye anachita zamphamvu ndi mkono wake; Iye anabalalitsa odzitama ndi mlingaliro wa mtima wao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201451 Iye anachita zamphamvu ndi mkono wake; Iye anabalalitsa odzitama ndi mlingaliro wa mtima wao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa51 Wachita zamphamvu ndi dzanja lake, wabalalitsa anthu a mtima wonyada. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero51 Iye wachita zamphamvu ndi dzanja lake; Iye anabalalitsa iwo amene ali onyada mʼmaganizo awo. Onani mutuwo |