Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 1:50 - Buku Lopatulika

50 Ndipo chifundo chake chifikira anthu a mibadwomibadwo pa iwo amene amuopa Iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

50 Ndipo chifundo chake chifikira anthu a mibadwomibadwo pa iwo amene amuopa Iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

50 Amaŵachitira chifundo anthu a mibadwo ndi mibadwo amene amamlemekeza.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

50 Chifundo chake chifikira kwa iwo amene amuopa Iye kufikira mibadomibado.

Onani mutuwo Koperani




Luka 1:50
15 Mawu Ofanana  

Ndipo ndidzalimbitsa pangano langa ndi Ine ndi iwe pa mbeu zako za pambuyo pako m'mibadwo yao, kuti likhale pangano la nthawi zonse, kuti ndikhale Mulungu wako ndi wa mbeu zako za pambuyo pako.


koma Yehova Mulungu wanu muzimuopa, nadzakulanditsani Iyeyu m'dzanja la adani anu onse.


Pakuti monga m'mwamba mutalikira ndi dziko lapansi, motero chifundo chake chikulira iwo akumuopa Iye.


Adzadalitsa iwo akuopa Yehova, aang'ono ndi aakulu.


Anene tsono iwo akuopa Yehova, kuti chifundo chake nchosatha.


Adzachita chokhumba iwo akumuopa; nadzamva kufuula kwao, nadzawapulumutsa.


Yehova akondwera nao akumuopa Iye, iwo akuyembekeza chifundo chake.


Ha! Kukoma kwanu ndiko kwakukulu nanga, kumene munasungira iwo akuopa Inu, kumene munachitira iwo akukhulupirira Inu, pamaso pa ana a anthu!


Indedi chipulumutso chake chili pafupi ndi iwo akumuopa Iye; kuti m'dziko mwathu mukhale ulemu.


ndi kuwachitira chifundo anthu zikwizikwi a iwo amene akondana ndi Ine, nasunga malamulo anga.


Chifukwa Iye Wamphamvuyo anandichitira ine zazikulu; ndipo dzina lake lili loyera.


Ndipo mau anachokera kumpando wachifumu, ndi kunena, Lemekezani Mulungu wathu akapolo ake onse akumuopa Iye, aang'ono ndi aakulu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa