Luka 1:49 - Buku Lopatulika49 Chifukwa Iye Wamphamvuyo anandichitira ine zazikulu; ndipo dzina lake lili loyera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201449 Chifukwa Iye Wamphamvuyo anandichitira ine zazikulu; ndipo dzina lake lili loyera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa49 pakuti Iye amene ali wamphamvu wandichitira zazikulu, ndipo dzina lake nloyera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero49 pakuti Wamkuluyo wandichitira ine zinthu zazikulu, dzina lake ndi loyera. Onani mutuwo |