Luka 1:48 - Buku Lopatulika48 chifukwa Iye anayang'anira umphawi wa mdzakazi wake; pakuti taonani, kuyambira tsopano, anthu a mibadwo yonse adzanditchula ine wodala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201448 chifukwa Iye anayang'anira umphawi wa mdzakazi wake; pakuti taonani, kuyambira tsopano, anthu a mibadwo yonse adzanditchula ine wodala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa48 popeza kuti wayang'ana kutsika kwa mtumiki wake. Ndithu kuyambira tsopano anthu a mibadwo yonse adzanditcha wodala, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero48 pakuti wakumbukira kudzichepetsa kwa mtumiki wake. Kuyambira tsopano mibado yonse idzanditcha wodala, Onani mutuwo |