Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 1:46 - Buku Lopatulika

46 Ndipo Maria anati, Moyo wanga ulemekeza Ambuye,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

46 Ndipo Maria anati, Moyo wanga ulemekeza Ambuye,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

46 Pamenepo Maria adati, “Mtima wanga ukutamanda Ambuye,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

46 Ndipo Mariya anati: “Moyo wanga ulemekeza Ambuye.

Onani mutuwo Koperani




Luka 1:46
15 Mawu Ofanana  

Ndipo moyo wanga udzakondwera mwa Yehova; udzasekera mwa chipulumutso chake.


Mwa Yehova mbeu yonse ya Israele idzalungamitsidwa ndi kudzikuza.


Ndidzakondwa kwambiri mwa Yehova, moyo wanga udzakondwerera mwa Mulungu wanga; pakuti Iye wandiveka ine ndi zovala za chipulumutso, nandifunda chofunda cha chilungamo, monga mkwati avala nduwira, ndi monga mkwatibwi adzikometsa yekha ndi miyala yamtengo.


Ndipo si chotero chokha, koma ife tikondwera ndi Mulungu mwa Ambuye wathu Yesu Khristu, amene talandira naye tsopano chiyanjanitso.


kuti monga mwalembedwa, Iye amene adzitamanda, adzitamande mwa Ambuye.


Koma ayamikike Mulungu, amene atitsogolera m'chigonjetso mwa Khristu, namveketsa fungo la chidziwitso chake mwa ife pamalo ponse.


pakuti ife ndife mdulidwe, akutumikira popembedza ndi Mzimu wa Mulungu, nadzitamandira mwa Khristu Yesu, osakhulupirira m'thupi;


Kondwerani mwa Ambuye nthawi zonse: ndibwerezanso kutero, kondwerani.


Ndipo Mulungu wa mtendere yekha ayeretse inu konsekonse; ndipo mzimu wanu ndi moyo wanu ndi thupi lanu zisungidwe zamphumphu, zopanda chilema pa kudza kwake kwa Ambuye wathu Yesu Khristu.


amene mungakhale simunamuone mumkonda; amene mungakhale simumpenya tsopano, pokhulupirira, mukondwera naye ndi chimwemwe chosaneneka, ndi cha ulemerero:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa