Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 1:44 - Buku Lopatulika

44 Pakuti ona, pamene mau a moni wako analowa m'makutu anga, mwana anatsalima ndi msangalalo m'mimba mwanga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

44 Pakuti ona, pamene mau a moni wako analowa m'makutu anga, mwana anatsalima ndi msangalalo m'mimba mwanga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

44 Chifukwatu pamene ndinamva malonje anu, mwana anayamba kutakataka ndi chimwemwe m'mimba mwanga.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

44 Nthawi yomwe ndinamva mawu akulonjera kwanu, mwana anatakataka mʼmimba mwanga chifukwa cha chimwemwe.

Onani mutuwo Koperani




Luka 1:44
4 Mawu Ofanana  

Ndipo panali pamene Elizabeti anamva kulonjera kwake kwa Maria, mwana wosabadwayo anatsalima m'mimba mwake; ndipo Elizabeti anadzazidwa ndi Mzimu Woyera;


Ndipo ichi chichokera kuti kudza kwa ine, kuti adze kwa ine amake wa Ambuye wanga?


Ndipo wodala ali iye amene anakhulupirira; chifukwa zidzachitidwa zinthu zimene Ambuye analankhula naye.


Kondwerani tsiku lomweli, tumphani ndi chimwemwe; pakuti onani, mphotho zanu nzazikulu Kumwamba; pakuti makolo ao anawachitira aneneri zonga zomwezo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa