Luka 1:43 - Buku Lopatulika43 Ndipo ichi chichokera kuti kudza kwa ine, kuti adze kwa ine amake wa Ambuye wanga? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201443 Ndipo ichi chichokera kuti kudza kwa ine, kuti adze kwa ine amake wa Ambuye wanga? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa43 Ine ndine yani kuti inu, mai wa Ambuye anga, mudzandiyendere? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero43 Koma nʼchifukwa chiyani andikomera mtima kuti amayi a Ambuye anga abwere kwa ine? Onani mutuwo |