Luka 1:42 - Buku Lopatulika42 nakweza mau ndi mfuu waukulu, nati, Wodalitsika iwe mwa akazi, ndipo chodalitsika chipatso cha mimba yako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201442 nakweza mau ndi mfuu waukulu, nati, Wodalitsika iwe mwa akazi, ndipo chodalitsika chipatso cha mimba yako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa42 ndipo adalankhula mokweza mau kuti, “Ndinu odala kupambana akazi ena onse, ngwodalanso Mwana wanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero42 Anafuwula ndi mawu akulu kuti, “Ndiwe wodala pakati pa akazi, ndipo ndi wodala mwana amene udzabereke! Onani mutuwo |