Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 1:38 - Buku Lopatulika

38 Ndipo Maria anati, Onani, mdzakazi wa Ambuye; kukhale kwa ine monga mwa mau anu. Ndipo mngelo anachoka kwa iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

38 Ndipo Maria anati, Onani, mdzakazi wa Ambuye; kukhale kwa ine monga mwa mau anu. Ndipo mngelo anachoka kwa iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

38 Apo Maria adati, “Ndine mtumiki wa Ambuye; zindichitikire monga mwaneneramo.” Ndipo mngeloyo adamsiya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

38 Mariya anayankha kuti, “Ine ndine mtumiki wa Ambuye. Zikhale kwa ine monga mwanenera.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 1:38
8 Mawu Ofanana  

Ndiloleni, Yehova, indetu ndine mtumiki wanu; ndine mtumiki wanu, mwana wa mdzakazi wanu; mwandimasulira zondimanga.


Limbitsirani mtumiki wanu mau anu, ndiye wodzipereka kukuopani.


Chifukwa palibe mau amodzi akuchokera kwa Mulungu adzakhala opanda mphamvu.


Ndipo Maria ananyamuka masiku amenewa, namuka ndi changu kudziko la mapiri kumzinda wa Yuda;


chifukwa Iye anayang'anira umphawi wa mdzakazi wake; pakuti taonani, kuyambira tsopano, anthu a mibadwo yonse adzanditchula ine wodala.


Pakuti palembedwa, kuti Abrahamu anali nao ana aamuna awiri, mmodzi wobadwa mwa mdzakazi, ndi mmodzi wobadwa mwa mfulu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa