Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 1:37 - Buku Lopatulika

37 Chifukwa palibe mau amodzi akuchokera kwa Mulungu adzakhala opanda mphamvu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

37 Chifukwa palibe mau amodzi akuchokera kwa Mulungu adzakhala opanda mphamvu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

37 Pajatu palibe kanthu kosatheka ndi Mulungu.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

37 Pakuti palibe chinthu chosatheka ndi Mulungu.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 1:37
14 Mawu Ofanana  

Kodi chilipo chinthu chomkanika Yehova? Pa nthawi yoikidwa ndidzabwera kwa iwe, pakufika nyengo yake, ndipo Sara adzakhala ndi mwana wamwamuna.


Mbiya ya ufa siidathe, ndi nsupa ya mafuta siinachepe, monga mwa mau a Yehova amene ananenetsa Eliya.


Ndipo ichi chidzapepuka pamaso pa Yehova; adzaperekanso Amowabu m'dzanja lanu.


Chimene muchidziwa inu, inenso ndichidziwa; sindikucheperani.


Ha! Yehova Mulungu, taonani, Inu munalenga kumwamba ndi dziko lapansi ndi mphamvu yanu yaikulu ndi mkono wanu wotambasuka; palibe chokanika Inu;


Taona, Ine ndine Yehova, Mulungu wa anthu onse; kodi kuli kanthu kondikanika Ine?


Atero Yehova wa makamu: Chikakhala chodabwitsa pamaso pa otsala a anthu awa masiku awo, kodi chidzakhalanso chodabwitsa pamaso panga? Ati Yehova wa makamu.


Ndipo Yehova anati kwa Mose, Kodi dzanja la Mulungu lafupikira? Tsopano udzapenya ngati mau anga adzakuchitikira kapena iai.


Ndipo Yesu anawayang'ana, nati kwa iwo, Ichi sichitheka ndi anthu, koma zinthu zonse zitheka ndi Mulungu.


Yesu anawayang'ana iwo nati, Sikutheka ndi anthu, koma kutheka ndi Mulungu; pakuti zinthu zonse zitheka ndi Mulungu.


Ndipo taona, Elizabeti mbale wako, iyenso ali ndi pakati pa mwana wamwamuna mu ukalamba wake; ndipo mwezi uno uli wachisanu ndi chimodzi wa iye amene ananenedwa wouma.


Ndipo Maria anati, Onani, mdzakazi wa Ambuye; kukhale kwa ine monga mwa mau anu. Ndipo mngelo anachoka kwa iye.


Koma Iye anati, Zinthu zosatheka ndi anthu zitheka ndi Mulungu.


amene adzasanduliza thupi lathu lopepulidwa, lifanane nalo thupi lake la ulemerero, monga mwa machitidwe amene akhoza kudzigonjetsera nao zinthu zonse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa