Luka 1:30 - Buku Lopatulika30 Ndipo mngelo anati kwa iye, Usaope, Maria; pakuti wapeza chisomo ndi Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Ndipo mngelo anati kwa iye, Usaope, Maria; pakuti wapeza chisomo ndi Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Mngeloyo adamuuza kuti, “Musaope, Maria, Mulungu wakukomerani mtima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Koma mngeloyo anati kwa iye, “Usachite mantha Mariya, pakuti wapeza chisomo pamaso Mulungu. Onani mutuwo |