Luka 1:31 - Buku Lopatulika31 Ndipo taona, udzakhala ndi pakati, nudzabala mwana wamwamuna, nudzamutcha dzina lake Yesu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Ndipo taona, udzakhala ndi pakati, nudzabala mwana wamwamuna, nudzamutcha dzina lake Yesu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Mudzatenga pathupi, ndipo mudzabala mwana wamwamuna. Mudzamutcha dzina lake Yesu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Udzakhala woyembekezera ndipo udzabala mwana wamwamuna ndipo udzamupatse dzina loti Yesu. Onani mutuwo |