Luka 1:24 - Buku Lopatulika24 Ndipo atatha masiku awa, Elizabeti mkazi wake anaima; nadzibisa miyezi isanu, nati, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndipo atatha masiku awa, Elizabeti mkazi wake anaima; nadzibisa miyezi isanu, nati, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Pambuyo pake mkazi wake Elizabeti adatenga pathupi, nabindikira miyezi isanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Zitatha izi, mkazi wake Elizabeti anakhala ndi pakati ndipo anadzibisa kwa miyezi isanu. Onani mutuwo |