Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 1:24 - Buku Lopatulika

24 Ndipo atatha masiku awa, Elizabeti mkazi wake anaima; nadzibisa miyezi isanu, nati,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Ndipo atatha masiku awa, Elizabeti mkazi wake anaima; nadzibisa miyezi isanu, nati,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Pambuyo pake mkazi wake Elizabeti adatenga pathupi, nabindikira miyezi isanu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Zitatha izi, mkazi wake Elizabeti anakhala ndi pakati ndipo anadzibisa kwa miyezi isanu.

Onani mutuwo Koperani




Luka 1:24
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Sara anatenga pakati, nambalira Abrahamu mu ukalamba wake mwana wamwamuna, nthawi yomweyo Mulungu anamuuza iye.


Ndipo mkaziyo anaima, naona mwana wamwamuna nyengo yomweyo chaka chimene chija Elisa adanena naye.


Ndipo kunali, pamene masiku a utumiki wake anamalizidwa, anamuka kunyumba kwake.


Ambuye wandichitira chotero m'masiku omwe Iye anandipenyera, kuchotsa manyazi anga pakati pa anthu.


Masiku a Herode, mfumu ya Yudeya, kunali munthu wansembe, dzina lake Zakariya, wa gulu la ansembe la Abiya; ndi mkazi wake wa ana aakazi a fuko la Aroni, dzina lake Elizabeti.


Taonani Teofilo inu, mau aja oyamba ndinakonza, za zonse Yesu anayamba kuzichita ndi kuziphunzitsa,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa