Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 1:23 - Buku Lopatulika

23 Ndipo kunali, pamene masiku a utumiki wake anamalizidwa, anamuka kunyumba kwake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Ndipo kunali, pamene masiku a utumiki wake anamalizidwa, anamuka kunyumba kwake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Atatha masiku ake otumikira m'Nyumba ya Mulungu, adapita kwao.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Nthawi yake yotumikira itatha, anabwerera kwawo.

Onani mutuwo Koperani




Luka 1:23
4 Mawu Ofanana  

Ndi abale ao m'midzi mwao akafikafika, atapita masiku asanu ndi awiri masabata onse, kuti akhale nao;


Koma m'mene iye anatulukamo, sanathe kulankhula nao; ndipo anazindikira kuti iye adaona masomphenya mu Kachisimo. Ndipo iye analinkukodola iwo, nakhalabe wosalankhula.


Ndipo atatha masiku awa, Elizabeti mkazi wake anaima; nadzibisa miyezi isanu, nati,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa