Luka 1:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo kunali, pamene masiku a utumiki wake anamalizidwa, anamuka kunyumba kwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo kunali, pamene masiku a utumiki wake anamalizidwa, anamuka kunyumba kwake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Atatha masiku ake otumikira m'Nyumba ya Mulungu, adapita kwao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Nthawi yake yotumikira itatha, anabwerera kwawo. Onani mutuwo |