Luka 1:2 - Buku Lopatulika2 monga anazipereka kwa ife iwo amene anakhala mboni ndi atumiki a mau, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 monga anazipereka kwa ife iwo amene anakhala mboni ndi atumiki a mau, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Iwo adalemba zimene adaatisimbira anthu oziwona chamaso kuyambira pachiyambi pake, nakhala akuzilalika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 monga mmene zinaperekedwera kwa ife ndi iwo amene anaona poyambirira ndi atumiki a mawu. Onani mutuwo |