Levitiko 9:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo ana a Aroni anasendera nao mwazi kwa iye; ndipo anaviika chala chake m'mwazimo naupaka pa nyanga za guwa la nsembe, nathira mwaziwo patsinde paguwa la nsembe; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo ana a Aroni anasendera nao mwazi kwa iye; ndipo anaviika chala chake m'mwazimo naupaka pa nyanga za guwa la nsembe, nathira mwaziwo patsinde pa guwa la nsembe; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Ndipo ana ake adapereka magazi kwa Aroni. Iyeyo adaviika chala chake m'magazimo, naŵapaka pa nyanga za guwa, nathira magaziwo patsinde pa guwa lomwelo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ana a Aaroni anabwera ndi magazi kwa Aaroni ndipo iye anaviyika chala chake mʼmagaziwo, nawapaka pa nyanga za guwa. Magazi wotsalawo anawathira pa tsinde la guwalo. Onani mutuwo |