Levitiko 9:8 - Buku Lopatulika8 Pamenepo Aroni anasendera kufupi kwa guwa la nsembe, napha mwanawang'ombe wa nsembe yauchimo, ndiyo ya kwa iye yekha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Pamenepo Aroni anasendera kufupi kwa guwa la nsembe, napha mwanawang'ombe wa nsembe yauchimo, ndiyo ya kwa iye yekha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Choncho Aroni adasendera pafupi ndi guwa, napha mwanawang'ombe woperekera nsembe yopepesera machimo, nsembeyo ya iye mwini wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Choncho Aaroni anasendera pafupi ndi guwa, napha mwana wangʼombe uja kukhala nsembe yake yopepesera machimo. Onani mutuwo |