Levitiko 9:10 - Buku Lopatulika10 koma mafutawo, ndi impso, ndi chokuta cha mphafa za nsembe yauchimo, anazitentha paguwa la nsembe; monga Yehova analamula Mose. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 koma mafutawo, ndi impso, ndi chokuta cha mphafa za nsembe yauchimo, anazitentha pa guwa la nsembe; monga Yehova anauza Mose. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Koma mafuta ndi imso, pamodzi ndi mphumphu ya mafuta akuchiŵindi, za nsembe yopepesera machimoyo, adazitenthera pa guwa, monga momwe Chauta adaalamulira Mose. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Kenaka anatentha paguwapo, mafuta, impsyo pamodzi ndi mafuta amene amakuta chiwindi ngati nsembe yopepesera machimoyo, monga momwe Yehova analamulira Mose. Onani mutuwo |