Levitiko 9:3 - Buku Lopatulika3 Nunene kwa ana a Israele, ndi kuti, Dzitengereni tonde akhale nsembe yauchimo; ndi mwanawang'ombe, ndi mwanawankhosa, a chaka chimodzi, opanda chilema, akhale nsembe yopsereza; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Nunene kwa ana a Israele, ndi kuti, Dzitengereni tonde akhale nsembe yauchimo; ndi mwanawang'ombe, ndi mwanawankhosa, a chaka chimodzi, opanda chilema, akhale nsembe yopsereza; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Tsono uuze Aisraele kuti, ‘Tengani tonde kuti muperekere nsembe yopepesera machimo. Mutengenso mwanawang'ombe ndi mwanawankhosa. Aŵiri onsewo akhale a chaka chimodzi, opanda chilema, kuti akhale nsembe yopsereza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Kenaka uwawuze Aisraeli kuti, ‘Tengani mbuzi yayimuna kuti ikhale nsembe yopepesera machimo. Mutengenso mwana wangʼombe ndi mwana wankhosa. Zonsezi zikhale za chaka chimodzi ndi zopanda chilema kuti zikhale nsembe yopsereza. Onani mutuwo |