Levitiko 9:4 - Buku Lopatulika4 ndi ng'ombe, ndi nkhosa yamphongo zikhale zakuyamika, kuziphera nsembe pamaso pa Yehova; ndi nsembe yaufa yosakaniza ndi mafuta; pakuti lero Yehova wakuonekerani inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 ndi ng'ombe, ndi nkhosa yamphongo zikhale zakuyamika, kuziphera nsembe pamaso pa Yehova; ndi nsembe yaufa yosanganiza ndi mafuta; pakuti lero Yehova wakuonekerani inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Mutengenso ng'ombe ndi nkhosa kuti zikhale nsembe zachiyanjano zoti aziphere pamaso pa Chauta. Mubwerenso ndi zopereka za zakudya zosakaniza ndi mafuta, pakuti lero Chauta akuwonekerani.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Mutengenso ngʼombe yayimuna ndi nkhosa yayimuna kuti zikhale nsembe yachiyanjano zoti ziperekedwe pamaso pa Yehova. Pamodzi ndi izi mubwerenso ndi nsembe yachakudya yosakaniza ndi mafuta pakuti lero Yehova akuonekerani.’ ” Onani mutuwo |