Levitiko 8:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo anamveka ndi malaya a m'kati, nammanga m'chuuno ndi mpango, namveka ndi mwinjiro, namveka ndi efodi, nammanga m'chuuno ndi mpango wa efodi nammanga nao pathupi pake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo anamveka ndi malaya a m'kati, nammanga m'chuuno ndi mpango, namveka ndi mwinjiro, namveka ndi efodi, nammanga m'chuuno ndi mpango wa efodi nammanga nao pathupi pake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Kenaka adamuveka mwinjiro Aroniyo, ndi kummanga lamba m'chiwuno. Adamuveka mkanjo ndi chovala cha efodi, ndipo adammanganso lamba wa efodiyo m'chiwuno. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Anamuveka Aaroni mwinjiro, ndi kumumanga lamba mʼchiwuno. Anamuvekanso mkanjo wa efodi ndi efodiyo. Anamangira lamba efodiyo amene analukidwa mwaluso uja, motero efodiyo analimba mʼchiwunomo. Onani mutuwo |