Levitiko 8:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo anamuika chapachifuwa; naika m'chapachifuwa Urimu ndi Tumimu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo anamuika chapachifuwa; naika m'chapachifuwa Urimu ndi Tumimu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Tsono adamuveka chovala chapachifuwa, ndipo m'chovalacho adaikamo zinthu zotchedwa Urimu ndi Tumimu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Anamuvekanso chovala chapachifuwa ndipo mʼchovalacho anayikamo Urimu ndi Tumimu. Onani mutuwo |