Levitiko 8:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo Mose anabwera nao Aroni ndi ana ake, nawasambitsa ndi madzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo Mose anabwera nao Aroni ndi ana ake, nawasambitsa ndi madzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Apo Mose adabwera ndi Aroni ndi ana ake, naŵasambitsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Pamenepo Mose anabwera ndi Aaroni ndi ana ake nawasambitsa ndi madzi. Onani mutuwo |